Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 12:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Nawonso akalonga a Farao anamuona ndipo anakauza Farao kuti mkaziyo ndi wokongola. Choncho mkaziyo anatengedwa nʼkupita naye kunyumba kwa Farao. 16 Farao anamusamalira bwino Abulamu chifukwa cha mkazi wake, moti anamupatsa nkhosa, ngʼombe, abulu aamuna ndi aakazi, antchito aamuna ndi aakazi komanso ngamila.+

  • Genesis 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Abulamu anali ndi chuma chambiri. Anali ndi ziweto, siliva ndi golide.+

  • Genesis 24:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano Abulahamu anali atakalamba ndipo anali ndi zaka zambiri. Yehova anali atamudalitsa mʼchilichonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena