Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 1:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Tsopano, pa nthawi imene oweruza+ ankatsogolera* ku Isiraeli, mʼdzikomo munagwa njala. Ndiyeno munthu wina anasamuka ku Betelehemu+ wa ku Yuda nʼkukakhala ngati mlendo ku Mowabu.+ Anasamuka ndi mkazi wake ndi ana ake awiri aamuna. 2 Munthuyu dzina lake anali Elimeleki,* ndipo mkazi wake anali Naomi.* Mayina a ana akewo anali Maloni* ndi Kiliyoni.* Anthuwa anali a ku Betelehemu Efurata wa ku Yuda. Ndipo anafika ku Mowabu nʼkumakhala kumeneko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena