Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsopano mtumiki wanga Davide ukamuuze kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Ine ndinakutenga kubusa kumene unkaweta nkhosa+ kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga.+

  • 2 Samueli 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ukadzamwalira+ nʼkugona mʼmanda ndi makolo ako, ndidzachititsa kuti mbadwa* yako, mwana wako weniweni, akhale mfumu ndipo ndidzachititsa kuti ufumu wake ukhazikike.+

  • 1 Mafumu 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komanso Yehova adzakwaniritsa zimene analonjeza zokhudza ineyo zakuti: ‘Ana ako akamadzachita zinthu mosamala komanso kuyenda mokhulupirika* pamaso panga ndi mtima wawo wonse ndi moyo wawo wonse,+ anthu a mʼbanja lako adzapitiriza kukhala pampando wachifumu wa Isiraeli.’+

  • 1 Mafumu 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 ndidzakhazikitsa mpando wako wachifumu mu Isiraeli mpaka kalekale, ngati mmene ndinalonjezera bambo ako Davide kuti, ‘Munthu wa mʼbanja lako sadzachoka pampando wachifumu wa Isiraeli.’+

  • Salimo 89:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndapeza Davide mtumiki wanga,+

      Ndipo ndamudzoza ndi mafuta anga opatulika.+

  • Salimo 89:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndidzachititsa kuti mbadwa* zake zidzakhalepo kwamuyaya,

      Ndipo ndidzachititsa kuti mpando wake wachifumu udzakhalepo mpaka kalekale ngati kumwamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena