Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 6:33-35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Adzangodzivulaza yekha ndipo anthu adzamunyoza,+

      Moti kunyozeka kwake sikudzafufutika.+

      34 Chifukwa nsanje imachititsa kuti mwamuna wake akwiye kwambiri.

      Pomubwezera sadzamva chisoni.+

      35 Iye sadzavomera chipukuta misozi chilichonse,*

      Ndipo sadzapepeseka ngakhale utapereka mphatso yaikulu bwanji.

  • Miyambo 7:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Iye akulondola mkaziyo mpaka muvi utaboola chiwindi chake,

      Ngati mbalame imene ikuthamangira kumsampha ndipo sakudziwa kuti zichititsa kuti ataye moyo wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena