Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 16:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mʼchaka cha 26 cha Asa mfumu ya Yuda, Ela mwana wa Basa anakhala mfumu ya Isiraeli ku Tiriza ndipo analamulira zaka ziwiri.

  • 1 Mafumu 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mʼchaka cha 27 cha Asa mfumu ya Yuda, Zimiri anakhala mfumu ku Tiriza ndipo analamulira masiku 7. Pa nthawiyo nʼkuti asilikali atamanga msasa pafupi ndi mzinda wa Gibitoni,+ umene unali wa Afilisiti, kuti amenyane ndi anthu amumzindawo.

  • 1 Mafumu 16:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma anthu amene ankatsatira Omuri anagonjetsa amene ankatsatira Tibini mwana wa Ginati. Choncho Tibini anafa ndipo Omuri anakhala mfumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena