Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 9:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Koma aliyense wokhumudwitsa mmodzi wa tiana iti timene tili ndi chikhulupiriro, zingamukhalire bwino kwambiri ngati atamumangirira chimwala champhero mʼkhosi mwake chimene bulu amayendetsa nʼkumuponya munyanja.+

  • Luka 17:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako Yesu anauza ophunzira ake kuti: “Nʼzosatheka kuti pakhale popanda zopunthwitsa. Koma tsoka kwa munthu amene zopunthwitsazo zimadzera mwa iye! 2 Zingamukhalire bwino kwambiri atamumangirira chimwala cha mphero mʼkhosi mwake nʼkumuponya mʼnyanja, kusiyana ndi kuti akhumudwitse mmodzi wa tiana iti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena