Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 9:35-37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yesu anamva kuti munthu uja amuchotsa musunagoge. Ndipo atakumana naye anamufunsa kuti: “Kodi ukukhulupirira Mwana wa munthu?” 36 Munthuyo anayankha kuti: “Kodi mwana wa munthuyo ndi ndani? Ndiuzeni bambo kuti ndimukhulupirire.” 37 Yesu anamuuza kuti: “Wamuona kale, ndipo ndi amene akulankhula nawe panopa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena