Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 2:28, 29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Amene ali Myuda kunja kokha si Myuda,+ ndiponso mdulidwe wakunja kokha wochitidwa pathupi, si mdulidwe.+ 29 Kukhala Myuda weniweni kuli mumtima+ ndipo mdulidwe wake umakhalanso wamumtima+ wochitidwa ndi mzimu, osati ndi malamulo olembedwa.+ Munthu woteroyo amatamandidwa ndi Mulungu, osati anthu.+

  • 1 Akorinto 7:18-20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kodi pali mwamuna amene anaitanidwa ali wodulidwa?+ Akhalebe wodulidwa. Nanga alipo amene anaitanidwa ali wosadulidwa? Asadulidwe.+ 19 Mdulidwe sutanthauza chilichonse ndipo kusadulidwa sikutanthauzanso chilichonse,+ koma chofunika nʼkusunga malamulo a Mulungu.+ 20 Aliyense akhalebe mmene analili pamene ankaitanidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena