LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w13 8/1 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
w13 8/1 masa. 1-2

Zamkati

August 1, 2013

Kodi Zamalisece—Zilibe Vuto?

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. All rights reserved.

NKHANI ZOPHUNZILA

SEPTEMBER 30, 2013–OCTOBER 6, 2013 | TSAMBA 8 • NYIMBO: 125, 66

Mwapatulidwa

Monga atumiki odzipeleka a Yehova, tapatulidwa kuti ticite utumiki wopatulika. M’nkhani ino, tidzapenda lemba la Nehemiya caputala 13. Tidzakambilana mfundo zinai zimene zingatithandize kuti tikhalebe oyela mwa kuuzimu.

OCTOBER 7-13, 2013 | TSAMBA 13 • NYIMBO: 119, 80

‘Musakwiile Yehova’

M’nkhani iyi tidzapenda zinthu zisanu zimene zingapangitse Mkristu wokhulupilika ‘kukwiila Yehova.’ (Miy. 19:3) Kenako tidzakambilana mozama njila zisanu zimene zingatithandize kupewelatu kuimba mlandu Yehova cifukwa ca mavuto athu.

OCTOBER 14-20, 2013 | TSAMBA 18 • NYIMBO: 124, 20

Ganizilanani ndi Kulimbikitsana

OCTOBER 21-27, 2013 | TSAMBA 23 • NYIMBO: 61, 43

Ganizilani za Mtundu wa Munthu Amene Muyenela Kukhala

Pa nkhani ziŵilizi, yoyamba ifotokoza zimene tiyenela kucita kuti tithandizane kukhalabe olimba mosasamala kanthu za mavuto amene tingakumane nao. Nkhani yaciŵili idzafotokoza zimene tingacite kuti tigonjetse ziyeso zimene Satana amagwilitsila nchito pofuna kuononga ubwenzi wathu ndi Mulungu.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

Kodi Zamalisece Zilibe Vuto? 3

Tsanzilani Cikhulupililo Cao—Anam’sunga“Pomupulumutsa Pamodzi ndi Anthu Ena 7” 28

Kuyankha Mafunso a m’Baibo 32

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani