LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp17 na. 1 masa. 1-2
  • Mungacite Ciani Kuti Mupindule na Zimene Muŵelenga m’Baibo?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mungacite Ciani Kuti Mupindule na Zimene Muŵelenga m’Baibo?
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
wp17 na. 1 masa. 1-2
Nsanja ya Mlonda, Na. 1, 2017 | Mungacite Ciani Kuti Mupindule na Zimene Muŵelenga m’Baibo?

Mungacite Ciani Kuti Mupindule na Zimene Muŵelenga m’Baibo?

Na. 1 2017

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

Magazini iyi si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene imacitika padziko lonse lapansi. Zopeleka zaufulu n’zimene zimathandiza kupititsa patsogolo nchito imeneyi.

Kuti mucite copeleka, pitani pa webusaiti ya www.jw.org.

Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika kusiyapo ngati taonetsa ina.

MAGAZINI ya Nsanja ya Mlonda, imalemekeza Yehova Mulungu, amene ndi Wolamulila wa cilengedwe conse. Imalimbikitsa anthu ndi uthenga wabwino wakuti posacedwa, Ufumu wa Mulungu udzacotsa zoipa zonse ndi kusintha dziko lapansi kukhala paradaiso. Imalimbikitsa anthu kukhulupilila Yesu Khiristu amene anatifela kuti tikapeze moyo wosatha, ndipo panthawi ino iye akulamulila monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu. Magaziniyi yakhala ikufalitsidwa kuyambila mu 1879 ndipo si yandale. Mfundo zake zonse n’zocokela m’Baibo.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani