LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 June tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 June tsa. 2

Zamkati

3 Kodi Mukumbukila?

WIKI YA JULY 31, 2017–AUGUST 6, 2017

4 Yehova Amatitonthoza m’Masautso Athu Onse

Tonse timakumana ndi mavuto. Koma Yehova amatitonthoza. Nkhani iyi idzafotokoza zinthu zofunika zimene zingatithandize kupeza citonthozo panthawi ino ndi mtsogolo.

WIKI YA AUGUST 7-13, 2017

9 Ikani Mtima Wanu pa Cuma Cauzimu

Nkhani iyi, idzatithandiza kudziŵa mmene tingaseŵenzetsela mfundo ya m’fanizo la Yesu la wamalonda amene anali kusakila ngale. Idzatithandizanso kudzipenda ndi kuona mmene ise patekha, timaonela utumiki wopulumutsa moyo umene Akhristufe tinapatsidwa, ndi coonadi cimene takhala tikuphunzila zaka zonsezi.

14 Musamaone Cabe Maonekedwe a Munthu

16 Kodi Mudzakambilana Kuti Muthetse Mkangano ndi Kulimbikitsa Mtendele?

21 “Udalitsike Cifukwa ca Kulingalila Bwino Kwako”

WIKI YA AUGUST 14-20, 2017

22 Muziika Maganizo Anu pa Nkhani Yaikulu

WIKI YA AUGUST 21-27, 2017

27 Muzicilikiza Ulamulilo wa Yehova

Cifukwa cotangwanika na zocitika pa umoyo, cingakhale cosavuta kuiŵala zinthu zofunika. Nkhani izi zidzatithandiza kumvetsa kufunika kwa ulamulilo wa Yehova ndi kudziŵa mmene tingaucilikizile.

32 Kodi Mudziŵa?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani