LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 February tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 February tsa. 2

Zamkati

WIKI YA APRIL 2-8, 2018

3 Tengelani Cikhulupililo ndi Kumvela kwa Nowa, Danieli, na Yobu

WIKI YA APRIL 9-15, 2018

8 Kodi Mumam’dziŵa Yehova Monga Mmene Nowa, Danieli, na Yobu Anam’dziŵila?

Nowa, Danieli ndi Yobu anakumana na mavuto ambili monga amene timakumana nawo masiku ano. Kodi n’ciani cinawathandiza kukhalabe okhulupilika ndi omvela? Kodi kum’dziwa bwino Yehova kunawathandiza bwanji kuti akhalebe na mtima wosagawanika? Nkhani ziŵilizi zidzayankha mafunso amenewa.

13 Mbili Yanga​—Zinthu Zonse N’zotheka kwa Yehova

WIKI YA APRIL 16-22, 2018

18 Kodi Kukhala Munthu Wauzimu Kumatanthauzanji?

WIKI YA APRIL 23-29, 2018

23 Pitani Patsogolo Monga Munthu Wauzimu

M’nkhani yoyamba, tidzakambilana tanthauzo la kukhala munthu wauzimu komanso zimene tingaphunzile pa zitsanzo za anthu auzimu. M’nkhani yaciŵili, tidzakambilana zimene tingacite kuti tikhale anthu auzimu ndi mmene kukhala munthu wauzimu kungatithandizile mu umoyo wathu wa tsiku na tsiku.

28 Cimwemwe—Khalidwe Locokela kwa Mulungu

31 Za M’nkhokwe Yathu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani