LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w19 February tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa JW.ORG

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa JW.ORG
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
w19 February tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa JW.ORG

TSANZILANI CIKHULUPILILO CAWO

Eliya—Anapilila Mpaka Pamapeto

Citsanzo ca Eliya ca kupilila mokhulupilika cingalimbitse cikhulupililo cathu pamene tikumana na mavuto.

(Pitani ku Chichewa, pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > KUKHULUPILILA MULUNGU.)

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

Sindinkachedwa Kupsa Mtima

Munthu wina amene kale anali m’gulu la zigaŵenga anasintha, ndipo amaona kuti kusintha kwake ni umboni wakuti Baibo ili na mphamvu yosintha anthu. Tsopano iye ali pa ubale wolimba na Mulungu.

(Pitani ku Chichewa, pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > MTENDELE KOMANSO MOYO WOSANGALALA.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani