LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w19 June tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw Laibulale Na Pa Jw.Org

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw Laibulale Na Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
w19 June tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa Jw Laibulale Na Pa Jw.Org

KODI ZINANGOCITIKA ZOKHA?

Luso la Dolphin Lozindikila Zinthu Mosavuta

Asayansi akuyesetsa kutengela luso la Dolphin lozindikila zinthu mosavuta, pofuna kupanga zipangizo zimene zingawathandize kudziŵa zimene zikucitika m’madzi.

Pa JW Laibulale, ku Chichewa, pitani pa PUBLICATIONS > ARTICLE SERIES > WAS IT DESIGNED?

Pa jw.org, ku Chichewa, pitani pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > BAIBULO KOMANSO SAYANSI > KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA

Mungathandize Bwanji Mwana Wanu Kuti Azikhoza Bwino Kusukulu?

Mwana wanu akamapanikizika, amayamba kukhala ndi nkhawa akakhala kusukulu ndiponso kunyumba. Makolo angadziŵe vuto limene likucititsa mwana wawo kuti asamakhoze bwino komanso mmene angamuthandizile.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani