LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w19 December tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
w19 December tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA

Ndingatani Kuti Ndizigawa Bwino Nthawi Yanga?

Mfundo 5 zimene zingakuthandizeni kuti muzipewa kuwononga nthawi yanu.

Pa jw.org, pitani ku Chichewa pa ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAM ATA > ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA.

KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

Guluu wa Kanyama Kochedwa Barnacle

Guluu wa kanyama kameneka amamata mwamphamvu kwambili kuposa guluu aliyense wopangidwa ndi anthu. Posacedwapa, asayansi atulukila zimene zimathandiza kuti kanyamaka kazimamatila kwambili pamalo pamene pali madzi.

Pa jw.org, pitani ku Chichewa pa ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > BAIBULO KOMANSO SAYANSI > KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani