LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/13 tsa. 4
  • Athandizeni Kukhala ‘Okhazikika m’Cikhulupililo’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Athandizeni Kukhala ‘Okhazikika m’Cikhulupililo’
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Tingatsogozele Phunzilo la Baibo Lotsogolela Munthu ku Ubatizo—Gawo 2
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Thandizani Maphunzilo Anu a Baibo Kuti Akakhale Ophunzila Obatizika
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Mmene Tingatsogozele Phunzilo la Baibo Lotsogolela Munthu ku Ubatizo—Gawo 1
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Monga Mpingo, Thandizani Maphunzilo a Baibo Kupita Patsogolo Kuti Akabatizike
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 12/13 tsa. 4

Athandizeni Kukhala ‘Okhazikika m’Cikhulupililo’

N’zosangalatsa kuona mmene Yehova amadalitsila nchito yosonkhanitsa, caka ciliconse anthu oposa 2,500 amabatizika. (Deut. 28:2) Nthawi zambili wophunzila akabatizika, wofalitsa amasiya kuphunzila naye ndi kuyamba kuphunzila ndi ena. Wophunzila nayenso angafune kusiya kuphunzila kuti azithela nthawi yoculuka mu ulaliki. Koma n’kofunika kuti ophunzila akhazikike m’cikhulupililo. Iwo ayenela ‘kuzikika’ ndi “kukhazikika m’cikhulupililo.” (Akol. 2:6, 7; 2 Tim. 3:12) Conco, wophunzila akabatizika, ayenela kupitilizabe kuphunzila mpaka kumaliza buku la Baibo Imaphunzitsa ndi lakuti Cikondi ca Mulungu.—Onani Utumiki Wathu wa Ufumu wa April 2011 patsamba 2.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani