LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsa. 2
  • July 3-9

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 3-9
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 July tsa. 2

July 3-9

EZEKIELI 11–14

  • Nyimbo 52 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Kodi Muli na Mtima wa Mnofu?”:(10 min.)

    • Ezek. 11:17, 18—Yehova analonjeza kubwezeletsa kulambila koona (w07 7/1 peji 11 pala. 4)

    • Ezek. 11:19—Yehova angatipatse mtima wolabadila citsogozo cake (w16.05 peji 17 pala. 9)

    • Ezek. 11:20—Yehova amafuna kuti tiziseŵenzetsa zimene timaphunzila

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Ezek. 12:26-28—Ni udindo wanji umene mavesiwa apeleka kwa atumiki a Yehova? (w07 7/1 peji 13 pala. 8)

    • Ezek. 14:13, 14—Tiphunzilapo ciani pakuchulidwa kwa anthu aŵa? (w16.05 peji 30 pala. 13; w07 7/1 peji 13 pala. 9)

    • Kodi imwe pacanu kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Ezek. 12:1-10

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Konzekelani Maulaliki a Mwezi Uno: (15 min.) Kukambilana “Maulaliki a Citsanzo.” Tambitsani vidiyo imodzi-imodzi, ndipo kambilanani zimene mwaphunzilapo.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 154

  • Zofunikila za Mpingo: (15 min.) Apo ayi, kambilanani zimene tiphunzilapo mu Buku Lapacaka. (yb17 peji 41-43)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 14 mapa. 15-23, ndi bokosi lobwelelamo“ Kodi Mumaona Kuti Ufumu wa Mulungu ndi Weniweni?”

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 43 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani