LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsa. 4
  • July 17-23

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 17-23
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 July tsa. 4

July 17-23

EZEKIELI 18-20

  • Nyimbo 21 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Kodi Yehova Akatikhululukila Macimo, Amawakumbukilanso?”: (10 min.)

    • Ezek. 18:19, 20—Munthu aliyense adzadziyankhila mlandu kwa Yehova pa zocita zake (w12 7/1 peji 18 pala. 2)

    • Ezek. 18:21, 22—Yehova ni wokonzeka kukhululukila olapa ndipo sawasungilanso cifukwa (w12 7/1 peji 18 pala. 3-7)

    • Ezek. 18:23, 32—Yehova amawononga oipa kokha akaona kuti salapa (w08 4/1 peji 8 pala. 4; w06 12/1 peji 27 pala. 11)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Ezek. 18:29—N’cifukwa ciani Aisiraeli anayamba kuona Yehova molakwika? Nanga ise tingapewe bwanji kutengela zimenezo? (w13 8/15 peji 11 pala. 9)

    • Ezek. 20:49—N’cifukwa ciani anthu anaganiza kuti Ezekieli anali ‘kunena miyambi’? Pali cenjezo lanji kwa ise? (w07 7/1 peji 14 pala. 3)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Ezek. 20:1-12

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) 1 Yoh. 5:19—Phunzitsani Coonadi. Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) Gen. 3:2-5—Phunzitsani Coonadi. Yalani maziko a ulendo wotsatila. (Onani mwb16.08 peji 8 pala. 2.)

  • Nkhani: (6 mineti kapena kucepelapo) w16.05 32-CN—Mutu Wake: Kodi Mpingo Ungaonetse Bwanji Kukondwela pa Cilengezo Cakuti Cite Wabwezedwa?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 77

  • “Kodi Mumadziimbabe Mlandu?”: (10 min.) Kukambilana. Yambani ndi kutambitsa vidiyo yakuti Muzicilikiza Malamulo a Yehova—Muzikhululuka.

  • Zimene Achinyamata Amadzifunsa—Kodi Ndizitani Ndikalakwitsa Zinazake (5 min.) Kukambilana nkhani yakuti: Zimene Achinyamata Amadzifunsa—Kodi Ndizitani Ndikalakwitsa Zinazake? Yambani mwa kuliza mbali yakuti “Kodi inuyo mungatani?”

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 15 mapa. 9-17

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 38 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani