LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 September tsa. 5
  • September 18-24

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • September 18-24
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 September tsa. 5

September 18-24

DANIELI 1-3

  • Nyimbo 131 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Kukhala Wokhulupilika kwa Yehova Kumabweletsa Madalitso” (10 min.)

    • [Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Danieli.]

    • Dan. 3:16-20—Anzake a Danieli anacilimikabe poyesedwa kuti ataye cikhulupilililo cawo kwa Yehova (w15 7/15 peji 25 mapa. 15-16)

    • Dan. 3:26-29—Kukhulupilika kwawo kunatamanditsa Yehova ndipo kunawabweletsela madalitso w13 1/15 peji 10 pala. 13

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Dan. 1:5, 8—N’cifukwa ciani Danieli na anzake atatu anaona kuti kudya zakudya zabwino za mfumu kungawadetse? (it-2 peji 382)

    • Dan. 2:44—N’cifukwa ciani Ufumu wa Mulungu udzaphwanya maulamulilo a padziko, oimilidwa na fano? (w12 6/15 peji 17, bokosi; w01 10/15 peji 6 pala. 4)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Dan. 2: 31-43

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) Yes. 40:22— Phunzitsani Coonadi—Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) Aroma 15:4—Phunzitsani Coonadi—Musiileni kakhadi kongenela pa JW. ORG.

  • Nkhani: (6 mineti kapena kucepelapo) w17.02 peji 29-30—Mutu Wake: Kodi Yehova Amapendelatu Mayeselo Amene Tingakwanitse Kuwapilila, Kenako N’kuwasankha Kuti Tikakumane Nawo?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 63

  • “Khalani Okhulupilika Pamene Mukuyesedwa”: (8 min.) Kukambilana.

  • “Khalanibe Okhulupilika Pamene M’bululu Wanu Wacotsedwa”: (7 min.) Kukambilana.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr “Cigawo 6-Kucilikiza Ufumu​—Kumanga Malo Olambilila ndi Kupeleka Thandizo Pakacitika Ngozi,” nkhani 18, mapa. 1-8

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 101 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani