LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsa. 4
  • Pitilizani Kufuna-funa Ufumu Coyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitilizani Kufuna-funa Ufumu Coyamba
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Njila Yoonetsela Kuyamikila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo—Mbali 2
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • 4 Kodi Tiyenela Kupemphela za Ciani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2010
  • Dzipelekeni Kuthandiza pa Nchito Zomanga za Gulu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 January tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MATEYU 6-7

Pitilizani Kufuna-funa Ufumu Coyamba

M’pemphelo lake la citsanzo, Yesu anaonetsa kuti zinthu zokhudzana na colinga ca Yehova na Ufumu wake, tifunika kuziika patsogolo mu umoyo wathu.

6:9-13

  • Yesu ali pampando wake wacifumu kumwamba

    Dzina la Mulungu

    Ufumu wa Mulungu

    Cifunilo ca Mulungu

  • Mkate

    Cakudya ca lelo

    Kukhululuka macimo

    Kutilanditsa m’mayeselo

Zinthu zina zokhudzana ndi Ufumu zimene ningazipemphelele ni:

  • Kupita patsogolo kwa nchito yolalikila

  • Mzimu woyela wa Mulungu kuti uthandize amene akuzunzidwa

  • Dalitso la Mulungu pa nchito zomanga-manga kapena makampeni a ulaliki

  • Nzelu za Mulungu na mphamvu zake kuti zitsogolele amene amatitsogolela

  • Zina

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani