LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 September tsa. 6
  • September 24-30

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • September 24-30
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 September tsa. 6

September 24-30

YOHANE 7-8

  • Nyimbo 12 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Yesu Analemekeza Atate Wake”: (10 min.)

    • Yoh. 7:15-18—Yesu amati akatamandidwa pa kaphunzitsidwe kake, anali kupeleka citamandoco kwa Yehova (cf mape. 100-101 mapa. 5-6)

    • Yoh. 7:28, 29—Yesu anati anatumiwa monga woimilako Mulungu, kuonetsa kuti anali wogonjela kwa Yehova

    • Yoh. 8:29—Yesu anauza omvela ake kuti nthawi zonse anali kucita zinthu zokondweletsa Yehova (w11 3/15 peji 11 pala. 19)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yoh. 7:8-10—Kodi Yesu anawanamiza acibale ake osakhulupilila? (w07 2/1 peji 6 pala. 4)

    • Yoh. 8:58 nwt-E—N’cifukwa ciani kothela kwa vesiyi kuli mau akuti “nakhala nilipo” m’malo mwa mau akuti “nilipo”? Nanga n’cifukwa ciani zimenezi n’zofunika? (“nakhala nilipo,” nwtsty mfundo younikila)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Yoh. 8:31-47

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Kubwelelako Kaciŵili: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndipo itanilani munthuyo ku misonkhano.

  • Kubwelelako Kacitatu: (3 min. olo kucepelapo) Sankhani mwekha lemba na kugaŵila cofalitsa cophunzitsila Baibo.

  • Phunzilo la Baibo: (6 min. olo kucepelapo) lv mapeji 9-10 mapa. 10-11

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 103

  • “Onetsani Khalidwe la Kudzicepetsa Monga Khristu”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani mavidiyo onse payokha-payokha.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 36

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 119 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani