LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 December tsa. 3
  • ‘Mboni Ziŵili’ Zinaphedwa, Kenako Zinakhalanso na Moyo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ‘Mboni Ziŵili’ Zinaphedwa, Kenako Zinakhalanso na Moyo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 December tsa. 3
Mboni ziŵili zochulidwa m’buku la Chivumbulutso zaimilila kutsogola kwa zoikapo nyale na mitengo ya maolivi

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | CHIVUMBULUTSO 10-12

‘Mboni Ziŵili’ Zinaphedwa, Kenako Zinakhalanso na Moyo

11:3-11

  • ‘Mboni Ziŵili’: Kagulu ka abale odzozedwa amene anali kutsogolela pamene Ufumu wa Mulungu unakhazikitsidwa mu 1914

  • Kuphedwa: Pambuyo polalikila kwa zaka zitatu na hafu ‘atavala ziguduli,’ iwo anaphedwa pamene anamangiwa, cakuti sanathenso kugwila nchito zawo

  • Kukhalanso na moyo: Cakumapeto kwa zaka zitatu na hafu zophiphilitsila, iwo anakhalanso na moyo pamene anatulutsidwa m’ndende na kuyambanso kutsogolela pa nchito yolalikila

Chivumbulutso 11:1, 2 limagwilizanitsa zocitika zimenezi na kuyendela komanso kuyeletsa kacisi wauzimu wofotokozedwa pa Malaki 3:1-3. Nthawi imene ulosi unakwanilitsidwa ionetsa: kuyeletsedwa kwa kacisi kucokela ca kumapeto kwa 1914 mpaka ca kuciyambi kwa 1919; zaka zitatu na hafu kapena masiku 1,260 kucokela ca kumapeto kwa caka ca 1914 mpaka ca kuciyambi kwa 1918; masiku atatu na hafu kucokela kuciyambi kwa 1918 mpaka kuciyambi kwa 1919.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani