LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w20 May tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
w20 May tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

ZOCHITIKA PA MOYO WA A MBONI ZA YEHOVA

“Ndimachita Zomwe Ndingakwanitse”

Ngakhale kuti ali ndi zaka pafu-pifupi 90, a Irma amalemba makalata ofotokoza mfundo za m’Baibo ndipo anthu ambili amakhudzidwa mtima kwambili akalandila makalatawa.

Pitani pa jw.org ku Chichewa, pa mbali yakuti ZOKHUDZA IFEYO > ZOCHITIKA PA MOYO WA A MBONI ZA YEHOVA > KUUZA ENA CHOONADI CHA M’BAIBULO.

ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA

Ndingatani Kuti Ndizikonda Masewera Olimbitsa Thupi?

Kuwonjezela pa kukhala ndi thanzi labwino, kodi maseŵela olimbitsa thupi angakuthandizeninso bwanji?

Pitani pa jw.org ku Chichewa, pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA > ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani