LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w24 July tsa. 32
  • Khalanibe Maso mwa Kuŵelenga Baibo Mwakhama

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalanibe Maso mwa Kuŵelenga Baibo Mwakhama
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
  • Nkhani Zofanana
  • Tengelani Citsanzo ca Danieli
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
w24 July tsa. 32

ZIMENE MUNGACITE PA PHUNZILO LA INU MWINI

Khalanibe Maso mwa Kuŵelenga Baibo Mwakhama

Ŵelengani Danieli 9:​1-19 kuti mudziŵe kufunika koŵelenga Baibo mwakhama.

Mvetsani nkhani yonse. Ni zinthu ziti zimene zinali zitangocitika kumene? Nanga zinamukhudza bwanji Danieli? (Dan. 5:29–6:5) Mukanamva bwanji mukanakhala Danieli?

Kumbani mozamilapo. Ni “mabuku opatulika” ati amene Danieli ayenela kuti anali kuŵelenga? (Dan. 9:​2, mawu a m’munsi; w11 1/1 22 ¶2) N’cifukwa ciyani Danieli anavomeleza macimo ake komanso a mtundu wa Isiraeli? (Lev. 26:​39-42; 1 Maf. 8:​46-50; dp 182-184) Kodi pemphelo la Danieli lionetsa bwanji kuti anali kukonda kuŵelenga Mawu a Mulungu mwakhama?—Dan. 9:​11-13.

Onani maphunzilo amene mutengapo. Dzifunseni kuti:

  • ‘Ningapewe bwanji kuceutsidwa na zocitika za m’dzikoli?’ (Mika 7:7)

  • ‘Ningapindule bwanji nikamaŵelenga Mawu a Mulungu mwakhama mmene Danieli anali kucitila?’ (w04 8/1 12 ¶17)

  • ‘Ni nkhani ziti zimene ningaŵelenge pa phunzilo la ine mwini zimene zinganithandize ‘kukhalabe maso’?’ (Mat. 24:​42, 44; w12 8/15 5 ¶7-8)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani