LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 1/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 1/15 masa. 1-2

Zamkati

January 2016

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MLUNGU WA FEBRUARY 29, 2016–MARCH 6, 2016

3 ‘Pitilizani Kukonda Abale’

Kodi lemba la caka ca 2016 ndi liti? Nanga tifunika kuganizila ciani tikamaona lembali caka cino? Nkhani iyi itithandiza kudziŵa zimene tingacite kuti tipindule ndi lemba la caka cino.

MLUNGU WA MARCH 7-13, 2016

9 Muzilimbikitsidwa ndi Mphatso ya Mulungu Yosatheka Kuifotokoza

Yehova watipatsa “mphatso yake yaulele, imene sitingathe n’komwe kuifotokoza.” (2 Akorinto 9:15) Kodi mphatso imeneyi n’ciani? Nanga imatilimbikitsa bwanji kutengela Kristu Yesu, kukonda abale athu, ndi kuwakhululukila ndi mtima wonse? Nkhaniyi iyankha mafunso amenewa. Ifotokozanso zinthu zina zimene tingacite pa nyengo ya Cikumbutso.

MLUNGU WA MARCH 14-20, 2016

14 Mzimu Umacitila Umboni Limodzi ndi Mzimu Wathu

MLUNGU WA MARCH 21-27, 2016

20 “Tipita Nanu Limodzi”

Nkhani ziŵilizi zifotokoza mmene munthu amadziŵila kuti wasankhidwa kuti akakhale kumwamba ndiponso cimene cimacitika munthuyo akadzozedwa. Tikambilananso mmene odzozedwa ayenela kudzionela ndi mmene ife tiyenela kumvela tikaona kuti ciŵelengelo ca anthu amene amadya mkate ndi kumwa vinyo pa Cikumbutso cikukwela.

MLUNGU WA MARCH 28, 2016–APRIL 3, 2016

27 Kugwila Nchito ndi Mulungu—Kumabweletsa Cimwemwe

Nthawi zonse, Yehova wakhala akupatsa ena mwai wogwila naye nchito pokwanilitsa colinga cake. Iye amafuna kuti uthenga wabwino ulalikidwe padziko lonse lapansi, ndipo watipatsa mwai wogwila naye nchitoyi. Nkhani imeneyi ikufotokoza cifukwa cake kugwila nchito ndi Mulungu kumatibweletsela cimwemwe cacikulu.

CITHUNZI CA PACIKUTO:

MADAGASCAR

Mpainiya akuŵelengela Baibulo munthu amene akuyendetsa ngolo mumsewu wa pakati pa mitengo ya Baobab ku Morondava, m’dziko la Madagascar

OFALITSA

29,963

MAPHUNZILO A BAIBULO

77,984

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO

135,122

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani