LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • g20 na. 2 tsa. 2
  • Mawu Oyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba
  • Galamuka!—2020
  • Nkhani Zofanana
  • N’cifukwa Ciani Zinthu Zoipa Zimacitikila Anthu Abwino?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Zinthu Zoipa N’zoculuka
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Galamuka!—2020
g20 na. 2 tsa. 2
Kucipatala. Dokotala akupeleka uthenga woipa kwa okwatilana amene aimilila pafupi na khomo loloŵela m’kati.

Mawu Oyamba

Aliyense wa ife amakhudzidwa na mavuto aakulu monga matenda, ngozi, matsoka a zacilengedwe, kapena zaciwawa.

Anthu amafuna kudziŵa cifukwa cake timavutika.

  • Ena amakamba kuti mavuto amabwela cifukwa zinalembedwelatu, conco amaona kuti palibe kweni-kweni zimene tingacite kuti tiwapewe.

  • Enanso amakamba kuti timavutika cifukwa ca zina zimene tinacita kumbuyoku mu umoyo uno, kapena mu umoyo wina tisanamwalile na kubadwanso.

Tsoka likacitika, anthu amakhala na mafunso ambili.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani