LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 98
  • Fesani Mbewu za Ufumu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Fesani Mbewu za Ufumu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Fesani Mbewu za Ufumu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 98

Nyimbo 98

Fesani Mbewu za Ufumu

(Mateyu 13:4-8)

1. Akapolonu a Yehova

Amene mwadzipereka,

Bwerani kuntchito ya ’Mbuye

Ndipo muzimutsanzira.

Muzifesa mbewu za cho’nadi

M’mitima ya omvetsera.

Mukakhulupirika kwa Mulungu

Inde mudzamulemekeza.

2. Mbewu zina zomwe mufesa

Zidzagweratu pamwala.

Zidzakuladi kwa kanthawi

Pambuyo pake n’kufota.

Minga ikatsamwitsa cho’nadi

Amatengeka ndi dziko.

Zina zidzapeza nthaka yachonde

Ndiponso zidzakula bwino.

3. Kuti ntchito iyende bwino

Khama lanu n’lofunika.

Mukaleza mtima ndi anthu

Angakhozedi kusintha.

Mwa kukhala atcheru mungathe

Kuwathetseradi mantha.

Mungakolole zipatso makumi

Atatu kapena kuposa

(Onaninso Mat. 13:19-23; 22:37.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani