LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 16
  • Thawirani ku Ufumu wa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Thawirani ku Ufumu wa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani Maso, Limbani, Khalani Amphamvu
    Imbirani Yehova
  • Khalani Maso, Cilimikani, Khalani Amphamvu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 16

Nyimbo 16

Thawirani ku Ufumu wa Mulungu

(Zefaniya 2:3)

1. Bwerani kwa Yehova ofatsanu,

Zinthu zolungamadi muchite.

Tsiku la Yehova likadzafika

Mwina mungadzabisike.

(KOLASI)

Thawirani ku ’fumu wa M’lungu,

Khalani mbali yake.

N’kumene mudzapeza chitetezo.

M’mvereni, musachedwe.

2. Anjala ya choonadi nonsenu

Mudzamva chisoni mpaka liti?

Bwerani kwa Yehova m’pulumuke

Pansi pa Yesu khalani.

(KOLASI)

Thawirani ku ’fumu wa M’lungu,

Khalani mbali yake.

N’kumene mudzapeza chitetezo.

M’mvereni, musachedwe.

3. Tukulani mitu mosangalala,

Onanitu Ufumu wayamba.

Landirani kuwala kwa Yehova,

Muopeni iye yekha!

(KOLASI)

Thawirani ku ’fumu wa M’lungu,

Khalani mbali yake.

N’kumene mudzapeza chitetezo.

M’mvereni, musachedwe.

(Onaninso Sal. 59:15; Miy. 18:10; 1 Akor. 16:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani