LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 18
  • Chikondi cha Mulungu N’chosatha

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Chikondi cha Mulungu N’chosatha
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Cikondi Cokhulupilika ca Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Cikondi Cosasintha ca Yehova N’ciani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Yesu Ali Pacitsime Ndi Mkazi
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Cikondi Cokhulupilika Cimam’kondweletsa Yehova—Nanga Imwe?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 18

Nyimbo 18

Chikondi cha Mulungu N’chosatha

(Yesaya 55:1-3)

1. Chikondi cha M’lungu.

Ndithudi ndi chachikulu.

Iye anapereka

Mwana wake kwa ife

Kuti tipeze moyo,

Tipepezenso chimwemwe.

(KOLASI)

Inu nonse aludzu,

Dzamweni kwaulere.

Madzi opatsa moyo;

N’chifundo cha M’lungu.

2. Chikondi cha M’lungu.

Ntchito zake ndi umboni.

Watikonda popatsa

Mwana wake Ufumu

Pokwanitsa pangano.

Ufumu wake wadza.

(KOLASI)

Inu nonse aludzu,

Dzamweni kwaulere.

Madzi opatsa moyo;

N’chifundo cha M’lungu.

3. Chikondi cha M’lungu.

Nafenso tichisonyeze.

Tithandize ofatsa,

Kufuna chilungamo.

Tilalike kwa onse,

Uthenga wotonthoza.

(KOLASI)

Inu nonse aludzu,

Dzamweni kwaulere.

Madzi opatsa moyo;

N’chifundo cha M’lungu.

(Onaninso Sal. 33:5; 57:10; Aef. 1:7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani