LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 39
  • Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mtendele Wathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mtendele Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Imbirani Yehova
sn nyimbo 39

Nyimbo 39

Mtendere Wathu Wamtengo Wapatali

(Yohane 14:27)

1. Tamandani Yehova

Wamtendereyo.

Nkhondo adzazithetsa

Mwa Mwana wake,

Ndipo adzapambana

Nkhondo yabwino

N’kubweretsa mtendere

Padziko lonse.

2. Ukali ndi mkangano,

Izi tasiya.

Mikondo ndi lupanga

Zonse tataya.

Tilitu pa mtendere

Ndi anthu onse.

Monga nkhosa za Yesu,

Ee, zamtendere.

3. Mtendere ndi chipatso

Chachilungamo,

Ndi nzeru yakumwamba,

Yomwe tipempha.

Tiyendebe m’njirayi,

Timaikonda,

Mtendere udzakhala

Padziko lonse.

(Onaninso Sal. 46:9; Yes. 2:4; Yak. 1:17, 18.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani