LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 12
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Lonjezo la Moyo Wamuyaya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khulupilila Coonadi Iwe Mwini
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 12

Nyimbo 12

Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha

(Salmo 37:29)

1. Mulungu watilonjeza

Moyo womwe sudzatha.

‘Ofatsa ’dzasangalala.’

Zidzachitikadi.

(KOLASI)

Tingakhale nawo

Moyo wosathawo,

Tikamayesetsa,

Tidzaupeza.

2. Paradaiso akubwera,

Anthu adzamasuka.

Padzakhaladi mtendere

Wochoka kwa M’lungu.

(KOLASI)

Tingakhale nawo

Moyo wosathawo,

Tikamayesetsa,

Tidzaupeza.

3. Akufa akadzauka,

Chisoninso chidzatha.

Yehova adzapukuta

Misozi yonseyi.

(KOLASI)

Tingakhale nawo

Moyo wosathawo,

Tikamayesetsa,

Tidzaupeza.

(Onaninso Yes. 25:8; Luka 23:43; Yoh. 11:25; Chiv. 21:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani