LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 73
  • Tizikondana Kwambiri Kuchokera Mumtima

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tizikondana Kwambiri Kuchokera Mumtima
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tizikondana ndi Mtima Wonse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Cikondi Cosasintha ca Yehova N’ciani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Mmene Tingalimbikitsile Cikondi Cathu pa Ena
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Cikondi ca Umulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 73

Nyimbo 73

Tizikondana Kwambiri Kuchokera Mumtima

(1 Petulo 1:22)

1. Tiyenera kukondana

Mochokeradi mumtima

Zimene zimapangitsa

Kuti tizikondwa.

Chikondi chili mumtima

Tifuna kuchisonyeza

Potero tidzatsanzira

Atate Yehova.

Mawu ndi ntchito zathu

Zisonyeze kukonda ’nzathu.

Osowa tithandize

N’zomwe tingakwanitse.

Tichitire’na ulemu

Pamene athedwa nzeru,

Ayi tisawanenetu.

Tidzakhulupirika,

Tidzagwirizanika.

2. Pamenetu tikondana

Sitikwiyirana msanga,

Tikhala osangalala,

Ndi kudalirana.

Tidzakhala ndi mabwenzi

Omwe tingadaliredi,

Ndi kumakondana zedi

Ndi kumasonkhana.

Tonse timalakwitsa

N’kulankhula mosaganiza,

Choncho ndikofunika

Chifundo kusonyeza.

Timafuna kudziwika

Monga anthu okondana.

Choncho M’lungu wakumwamba

Tidzamulemekeza,

Inde kumutsanzira.

(Onaninso 1 Pet. 2:17; 3:8; 4:8; 1 Yoh. 3:11.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani