LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 107
  • Bwerani Kuphiri la Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Bwerani Kuphiri la Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Bwelani ku Phili la Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Funani Cipulumutso ca Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 107

Nyimbo 107

Bwerani Kuphiri la Yehova

(Yesaya 2:2-4)

1. Phiri la Yehova

Tangoliyang’anani,

Latalika kuposa

Ena onse lero.

Anthu akubwera

Kuchokera kutali,

Akuitanizana,

‘Bwerani kwa M’lungu.’

Tsopano wamng’ono

Wakhala mtundu waukulu.

Tikuona kuti

Tikudalitsidwa ndi M’lungu.

Ambiri tsopano

Akuvomerezadi

Ulamuliro wake

Mokhulupirika.

2. Yesu walamula

Kuti tipite ndithu

Tikalalikire

Uthenga wa Ufumu.

Khristu wayambano

Ulamuliro wake,

Ndipo akuti tikhale

Kumbali yake.

Ndi zosangalatsa

Kuona khamu lalikulu

Likukulirabe.

Ndipo tonse tikuthandiza.

Tonse tifuule

Anthu onsetu amve,

‘Bwerani anthuni

Kuphiri la Yehova.’

(Onaninso Sal. 43:3; 99:9; Yes. 60:22; Mac. 16:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani