LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 113
  • Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tiyamikila Mau a Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Muziyamika pa Ciliconse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Imbirani Yehova
sn nyimbo 113

Nyimbo 113

Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake

(Afilipi 2:16)

1. Yehova Atate, tikuyamika

Chifukwa mawu anu mwatipatsa.

Munauzira anthu kulemba za inu.

Malemba ’matitsogolera ndithu.

2. Aneneri anu anali anthu,

Ankamvadi mmene timamveratu.

Ndipo za moyo wawo tikamaphunzira

Timakhala anthu olimba mtima.

3. Mawu anu amatikhudza mtima.

Moyo ndi mzimu amalekanitsa.

Afufuza zolinga za mumtima wathu.

Atithandiza kukhala ndi nzeru.

(Onaninso Sal. 119:16, 162; 2 Tim. 3:16; Yak. 5:17; 2 Pet. 1:21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani