LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 76
  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Ndi Mulungu Wamtendere
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova, Mulungu wa Mtendele
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mtendele Kodi Mungaupeze Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Imbirani Yehova
sn nyimbo 76

Nyimbo 76

Yehova Ndi Mulungu Wamtendere

(Afilipi 4:9)

1. M’lungu wamtendere

M’tithandize tikhale

Ndi mtendere,

Makhalidwe abwino achuluke.

Malangizo anu,

Alowe mumtimamu.

Tikukupemphani

Mutipatse mtendere wanu.

2. Anthu m’dziko lonse

Akusowa mtendere.

Koma mtendere

Monga mvula muwazira ife.

Uchulukitseni

Ndipo tidalitseni.

Chifuniro chanu

Tikufuna tichidziwedi.

3. Mumatithandiza,

Mumatiunikira.

Mawu anu,

Mzimu wanu, zimatitsogolera.

Mtendere wangati

Mame ochulukadi.

Utitsitsimule,

Ukhazikitse mtima pansi.

(Onaninso Sal. 4:8; Afil. 4:6, 7; 1 Ates. 5:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani