LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 57
  • Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kusinkha-sinkha kwa Mtima Wanga
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pitilizani Kusinkhasinkha Zinthu za Kuuzimu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Imbirani Yehova
sn nyimbo 57

Nyimbo 57

Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga

(Salimo 19:14)

1. Zomwe ndimasinkhasinkha,

Zimene ndimaganiza,

Zikukondweretseni Ya

Kuti ndikhale wolimba.

Pamene ndili ndi nkhawa

N’kumalephera kugona

Ndisinkhesinkhe za inu,

Inde zinthu zoyenera.

2. Zilizonse zolungama,

Zofunika ndi zoona,

Ndikamaziganizira

Zindipezetse mtendere.

Nzeru zanu n’zofunika

Komanso ndi zochuluka.

Choncho ndizisinkhasinkha

Zonena zanu mwakhama.

(Onaninso Sal. 49:3; 63:6; 139:17, 23; Afil. 4:7, 8; 1 Tim. 4:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani