LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • ll gao 1 masa. 4-5
  • Kodi Tingamumvetsele Bwanji Mulungu?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Tingamumvetsele Bwanji Mulungu?
  • Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
  • Nkhani Zofanana
  • Gao 1
    Mvetselani kwa Mulungu
  • Baibulo Ni Buku Yocokela Kwa Mulungu
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Kodi Coonadi Cikali Cofunika Masiku Ano?
    Nkhani Zina
  • Kodi Baibo Imatiphunzitsanji za Mwiniwake wa Mawu a m’Bukulo?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Onaninso Zina
Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
ll gao 1 masa. 4-5

GAO 1

Kodi Tingamumvetsele Bwanji Mulungu?

Mulungu amakamba ndi ife kupitila m’Baibo. 2 Timoteyo 3:16

Kucokela ku mpando wake wacifumu kumwamba, Yehova akuuzila anthu kuti alembe Baibo

Mulungu woona anauza amuna ena kulemba maganizo ake m’buku lapadela. Buku limenelo ni Baibo. M’Baibo muli uthenga wofunika umene Mulungu afuna kuti mudziŵe.

Mulungu amadziŵa zinthu zabwino kwa ife ndipo ni Kasupe wa nzelu. Ngati mumvetsela kwa iye, mudzakhala anzelu.—Miyambo 1:5.

Mabaibo a zitundu zambili; munthu aŵelenga Baibo ya citundu cake

Mulungu afuna kuti aliyense padziko lapansi aziŵelenga Baibo. Ndipo masiku ano Baibo ili m’zitundu zambili.

Kuti mumvetsele kwa Mulungu, muyenela kuŵelenga Baibo ndi kuimvetsetsa.

Anthu kulikonse akuphunzila za Mulungu. Mateyu 28:19

Wa Mboni za Yehova akuŵelengela lemba munthu, kenako akuphunzila naye Baibo

Mboni za Yehova zingakuthandizeni kumvetsetsa Baibo.

Zimaphunzitsa coonadi ca Mulungu padziko lonse.

Anthu ali pa msonkhano mu Nyumba ya Ufumu ya Mboni za Yehova

Simufunika kulipila ndalama iliyonse kuti muphunzile coonadi. Ndiponso mungaphunzile za Mulungu ku Nyumba ya Ufumu ya Mboni za Yehova ya kumene mumakhala.

  • Mau a Mulungu ni coonadi.—Yohane 17:17.

  • N’cifukwa ciani tiyenela kukhulupilila Mulungu?—Numeri 23:19.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani