LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • ll gao 11 masa. 24-25
  • Kodi Yehova Amamvetsela kwa Ife?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Yehova Amamvetsela kwa Ife?
  • Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
  • Nkhani Zofanana
  • Mwayi Wa Pemphelo
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Muyandikileni Mulungu Kupitila m’Pemphelo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Mungapemphele Bwanji Kuti Mulungu Azimva Mapemphelo Anu?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2021
  • Gao 11
    Mvetselani kwa Mulungu
Onaninso Zina
Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
ll gao 11 masa. 24-25

GAO 11

Kodi Yehova Amamvetsela kwa Ife?

Mulungu amamva mapemphelo athu. 1 Petulo 3:12

Mpando wacifumu wa Yehova kumwamba

Yehova amamva mapemphelo. (Salimo 65:2) Amafuna kuti tizikamba naye kucokela mumtima.

Munthu apemphela

Muzipemphela kwa Yehova osati kwa wina aliyense.

  • Yesu anatiphunzitsa mmene tingapemphelele.—Mateyu 6:9-15.

  • Kodi Mulungu amamvetsela kwa ndani?—Salimo 145:18, 19.

Tingapemphelele zinthu zambili. 1 Yohane 5:14

Yesu pamodzi ndi a 144,000 mu Ufumu wa Mulungu

Muzipemphela kuti cifunilo ca Mulungu cicitike kumwamba ndi pano padziko.

Muzipemphela m’dzina la Yesu, kuonetsa kuti mumayamikila zimene anakucitilani.

Mkhristu adalila Yehova kuti apeze zosoŵa zake ndi za banja lake ndiponso kuti  acite zabwino

Muzipempha Yehova kuti akuthandizeni kucita zabwino. Ndiponso mungapemphe za cakudya, nchito, nyumba, zovala, ndi thanzi lanu.

  • Yehova amamvetsela kwa anthu amene amacita zinthu zabwino.—Miyambo 15:29.

  • Musadele nkhawa.—Afilipi 4:6, 7.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani