LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mb phunzilo 1
  • Phunzilo 1

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzilo 1
  • Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
Zimene Ndimaphunzila m’Baibo
mb phunzilo 1

Phunzilo 1

Chivumbulutso 4:11

Ndani anapanga dziko?

Ndani anapanga nyanja?

Ndani anapanga iwe ndi ine?

Ndani anapanga gulugufe ndi mapiko ake okongola?

Yehova Mulungu analenga zinthu zonse.

ZOCITA

Muŵelengeleni mwana wanu:

Chivumbulutso 4:11

Uzani mwana wanu kuti aloze:

Nyenyezi Mitambo Dzuŵa

Boti Dziko Nyumba

Nyanja Gulugufe

M’funseni mwana wanu:

Dzina la Mulungu ndani?

Yehova akhala kuti?

Anapanga ciani?

[Cithunzi 4, 5]

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani