LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb tsa. 240
  • Maphunzilo amene tingatengemo m’Baibo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maphunzilo amene tingatengemo m’Baibo
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Cigawo 4
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Lipoti la Maiko na Madela
    Lipoti la Caka ca Utumiki ca 2021 la Mboni za Yehova Padziko Lonse
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb tsa. 240

Maphunzilo amene tingatengemo m’Baibo

KUCOKELA M’NKHANI IZI

Acicepele, tumikilani Yehova na mtima wonse 37, 51, 59, 61, 72, 100

Akufa adzauka 48, 86, 91, 93

Anthu oipa sadzakhalakonso 5, 10, 32, 46, 102

Anthu onse ni ofunika kwa Yehova 8, 9, 11, 21, 23, 68, 70, 74, 87, 90

Anthu opanduka amakhala adani a Mulungu 7, 17, 26, 27, 28, 88

Cifunilo ca Mulungu cicitike kumwamba na pa dziko lapansi 25, 55, 60, 62, 63, 71, 96, 102

Kudzikonda kungativulaze ife, na kuvulazanso anthu ena 3, 4, 12, 27, 28, 39, 49, 88

Kulambila konama kumacokela kwa Satana 19, 20, 22, 38, 46, 49, 52, 58

Limbani mtima, Yehova adzakuthandizani nthawi zonse 40, 47, 51, 53, 57, 61, 64, 65, 76, 88, 101

Mabwenzi abwino koposa ni amene amakonda Yehova 16, 33, 42, 80, 87, 100, 103

Mkwiyo ni woipa 4, 12, 41, 45, 49, 65, 89

Moyo wanu umadalila pa kukhala womvela 3, 5, 10, 37, 39, 54, 59, 65, 72

Mulungu anatipatsa Baibo kuti tikhale anzelu 56, 66, 72, 75, 81

Musataye mtima pokumana na mavuto 16, 47, 51, 57, 64, 75, 90, 95, 99, 101

Muzikhululukila ena mmene Yehova amacitila kwa imwe 13, 15, 31, 43, 92

Muzikwanilitsa malonjezo anu mmene Yehova amacitila 8, 9, 11, 23, 24, 31, 34, 35, 36, 66, 93

Muziyamikila Yehova nthawi zonse 2, 6, 67, 103

Ngati simukonda m’bale wanu, simungakonde Mulungu 4, 13, 15, 41

Nsanje imawononga ubwenzi 4, 14, 41

Pangani Yehova kukhala bwenzi lanu 11, 30, 33, 51, 56, 59, 69, 81, 82

Pewani kucita zoipa 14, 27, 49, 53, 58, 88, 89

Sitingatumikile Mulungu na Cuma pa nthawi imodzi 10, 17, 44, 59, 75, 76

Tetezani zimene Yehova wakupatsani 12, 13, 24, 35, 36, 56, 75, 95, 100

Tifunika kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu 73, 76, 94, 95, 96, 97, 98

Ufumu wa Mulungu udzabweletsa cimwemwe kwa aliyense 1, 48, 62, 79, 81, 83, 85, 86

Yehova amakonda anthu a mitundu yonse 30, 33, 48, 54, 77, 94, 97, 98, 99

Yehova amamvela mapemphelo athu ocokela pansi pa mtima 35, 38, 50, 64, 82

Yehova amateteza anthu amene amam’konda 6, 22, 40, 50, 52, 55, 64, 71, 84

Yehova amateteza anthu odzicepetsa 43, 45, 65, 67, 69

Yehova amatsogolela anthu ake 18, 25, 26, 27, 29, 34, 39, 44, 73, 80

Yehova anatipangila dziko lapansi kuti tikhalepo 1, 2, 102, 103

Yehova ni wamphamvuzonse 1, 7, 18, 19, 20, 21, 22, 26, 55, 60

Yehova sanama 3, 10, 16, 63, 68, 70, 102, 103

Yehova sangaiŵale zimene timam’citila 16, 29, 32, 48, 65, 69, 77, 100

Yesu ni Mfumu ya Ufumu wa Mulungu—mumveleni 74, 78, 79, 83, 84, 85, 91, 92, 99

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani