LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 136-137
  • Mawu Oyamba a Cigawo 10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 10
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Iwo Sanagwadile Fano
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Anakana Kugwadila Fano
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Danieli Mu Dzenje La Mikango
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Kucokela pa Ukapolo ku Babulo, Kukafika pa Kumangidwanso kwa Mpanda wa Yerusalemu
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 136-137
Mfumu Ahasiwero ilata Mfumukazi Esitere na ndodo yake yacifumu

Mawu Oyamba a Cigawo 10

Yehova ni Mfumu ya cilengedwe conse. Iye nthawi zonse wakhala akulamulila, ndipo adzalamulilabe kwamuyaya. Mwacitsanzo, anapulumutsa Yeremiya m’citsime cozama. Anapulumutsa Sadirake, Mesake na Abedinego m’ng’anjo ya moto, komanso Danieli m’dzenje la mikango. Yehova anateteza Esitere kuti apulumutse anthu onse a mtundu wake. Iye sadzalola kuti zoipa zipitilize kwamuyaya. Maulosi okhudza fano lalikulu komanso mtengo waukulu, amatitsimikizila kuti Ufumu wa Yehova posacedwa udzacotsapo zoipa zonse na kuyamba kulamulila pa dziko lapansi.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Ufumu wa Yehova ni wamphamvu kwambili kuposa boma iliyonse ya anthu

  • Potengela citsanzo ca Esitere na Danieli, nthawi zonse tifunika kulimba mtima kuti ticite coyenela kulikonse kumene tingakhale

  • Tifunika kudalila Yehova na mtima wonse tikakumana na mavuto, monga mmene anacitila Yeremiya na Nehemiya

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani