LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 41
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • N’dzayenda mu Umphumphu Wanga
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pemphelo la Munthu Wovutika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 41

NYIMBO 41

Mvelani Pemphelo Langa Conde

Yopulinta

(Salimo 54)

  1. 1. Nidzakutamandani M’lungu.

    Imwe ndimwe Atate wanga.

    Dzina lanu ni lalikulu.

    (KOLASI)

    Conde Yehova, nimveleni.

  2. 2. Nikuyamikani Yehova.

    Mwanipatsa mphatso ya moyo.

    Imwe mumanisamalila.

    (KOLASI)

    Conde Yehova, nimveleni.

  3. 3. M’lungu wanga nithandizeni,

    Nipilile mavuto onse.

    Nifuna kucita zabwino.

    (KOLASI)

    Conde Yehova, nimveleni.

(Onaninso Eks. 22:27; Sal. 106:4; Yak. 5:11)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani