LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 105
  • “Mulungu Ndiye Cikondi”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Mulungu Ndiye Cikondi”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
  • Cikondi Khalidwe Lamtengo Wapatali
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Musalole Kuti Cikondi Canu Cizilale
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 105

NYIMBO 105

“Mulungu Ndiye Cikondi”

Yopulinta

(1 Yohane 4:7, 8)

  1. 1. Mulungu ndiye cikondi,

    Tikhale monga iye.

    Tikakhala na cikondi

    Iye adzatiyanja.

    Tidzapeza madalitso,

    Tidzapeza cimwemwe.

    Monga otsatila Khristu

    Tionetse cikondi.

  2. 2. Ngati tikonda Yehova

    Tidzacita zabwino.

    Iye adzatiphunzitsa

    Kukhala acikondi.

    Cikondi citilimbitsa

    Potumikila M’lungu.

    Tikakhala na cikondi,

    Sitidzacita nsanje.

  3. 3. Tisabwezele coipa,

    Tikhale acifundo.

    Tikonde abale athu,

    Tikhale monga M’lungu.

    Ngati ena ‘tilakwila

    Tiŵakhululukile.

    Mu zocita zathu zonse

    Tikhale acikondi.

(Onaninso Maliko 12:30, 31; 1 Akor. 12:31–13:8; 1 Yoh. 3:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani