LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp17 na. 3 tsa. 2
  • Mau Oyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mau Oyamba
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
  • Nkhani Zofanana
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Mmene Amuna Anayi Okwela pa Mahosi Amakukhudzilani
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
  • Amuna Anayi Okwela pa Mahosi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhondo ya ku Ukraine Iwonjezela Njala Padziko Lonse
    Nkhani Zina
Onaninso Zina
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
wp17 na. 3 tsa. 2

Mau Oyamba

MUGANIZA BWANJI?

Nkhani ya amuna anayi okwela pa mahosi ni imodzi mwa nkhani zodziŵika kwambili m’buku la Chivumbulutso. Anthu ena amacita nayo mantha. Ena amacita nayo cidwi. Onani zimene Baibo imakamba zokhudza maulosi monga amenewa:

“Wodala ndi munthu amene amaŵelengela ena mokweza, ndiponso anthu amene akumva mau a ulosi umenewu.”—Chivumbulutso 1:3.

Magazini iyi ya Nsanja ya Mlonda, ifotokoza mmene tingapindulile na nkhani ya amuna anayi okwela pa mahosi.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani