LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsa. 3
  • Kukonzekela n’Kofunika Kuti Tiziphunzitsa Mwaluso

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kukonzekela n’Kofunika Kuti Tiziphunzitsa Mwaluso
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Tingatsogozele Phunzilo la Baibo Lotsogolela Munthu ku Ubatizo—Gawo 1
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Thandizani Maphunzilo Anu a Baibo Kuti Akakhale Ophunzila Obatizika
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Motsogozela Phunzilo la Baibo Poseŵenzetsa Buku la “Kondwelani na Moyo Kwamuyaya!”
    Kondani Anthu Kuti Mupange Ophunzila
  • Mmene Tingatsogozele Phunzilo la Baibo Lotsogolela Munthu ku Ubatizo—Gawo 2
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsa. 3

Kukonzekela n’Kofunika Kuti Tiziphunzitsa Mwaluso

Yesu anafunsidwa funso lokhudza moyo wosatha kaŵili konse. Koma panthawi zonsezi, iye anayankha mogwilizana ndi zosoŵa za wofunsayo. (Luka 10:25-28; 18:18-20) Ngakhale kuti timalidziŵa bwino buku lophunzilila Baibulo, tifunika kukonzekelabe tili ndi wophunzila m’maganizo mwathu. Kodi ndi mfundo ziti zimene angavutike kumvetsetsa kapena kuzivomeleza? Ndi malemba ati amene tidzaŵelenga naye? Nanga tidzaphunzila zinthu zoculuka motani? Mwina tingafunike kukonzekela fanizo, mmene tidzafotokozela mfundo inayake kapena mafunso angapo kuti tithandize wophunzila kumvetsetsa nkhaniyo. Popeza Yehova ndi amene amakulitsa mbeu za coonadi mumtima mwa munthu, tifunika kum’pempha kuti atithandize pokonzekela phunzilo. Tifunikanso kum’pempha kuti athandize wophunzila wathu, ndi kuti adalitse khama lathu pothandiza wophunzilayo mwakuuzimu.​—1 Akor. 3:6; Yak. 1:5.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani