LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/15 tsa. 3
  • Bokosi La Mafunso

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Bokosi La Mafunso
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuleka Kutsogoza Maphunzilo a Baibo Osapita Patsogolo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Kulimba Mtima
    Kondani Anthu Kuti Mupange Ophunzila
  • Athandizeni Kukhala ‘Okhazikika m’Cikhulupililo’
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Mmene Tingatsogozele Phunzilo la Baibo Lotsogolela Munthu ku Ubatizo—Gawo 1
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 12/15 tsa. 3

Bokosi La Mafunso

◼ Ndi Liti Pamene Tingaleke Kuphunzila Baibulo Ndi Munthu Wina?

Tikaona kuti wophunzila Baibulo sapita patsogolo mwakuuzimu, mwanzelu tingaleke kuphunzila naye. (Mat. 10:11) Ganizilani izi: Kodi wophunzilayo amapezeka panthawi imene munapangana kuti muziphunzila? Kodi amakonzekela zimene mudzaphunzila kukali nthawi? Kodi amapezeka pa misonkhano ina ya mpingo? Kodi amauzako ena zimene amaphunzila? Kodi akusintha umoyo wake mogwilizana ndi mfundo za m’Baibulo? Komabe, tiyenela kuzindikila kuti anthu amapita patsogolo mosiyanasiyana malinga ndi msinkhu wao ndiponso maluso ao. Ndipo ngati mwasankha kuleka kuphunzila naye Baibulo, muuzeni kuti ndi womasuka kudzayambanso kuphunzila mtsogolo.—1 Tim. 2:4.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani