LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 April tsa. 4
  • Yobu Anapewa Maganizo Olakwika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yobu Anapewa Maganizo Olakwika
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • “Yembekezela Yehova”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yobu Anakhalabe Wokhulupilika Pamene Anali Kuyesedwa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 April tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YOBU 21-27

Yobu Anapewa Maganizo Olakwika

Yobu atseka khutu lake

Satana amaseŵenzetsa mabodza pofuna kufooketsa atumiki a Yehova masiku ano. Onani mmene mabodza a Satana amasiyanilana ndi mmene Yehova amaonela zinthu, malinga ndi mmene buku la Yobu likuonetsela. Lembani mndandanda wa Malemba ena oonjezela amene angakuthandizeni kuona kuti Yehova amakusamalilani.

MABODZA A SATANA

MMENE YEHOVA AMAONELA ZINTHU

Mulungu ndi wovuta kwambili kumusangalatsa, cakuti palibe ciliconse cimene atumiki ake amacita cimene iye amasangalala naco. Ngakhale cilengedwe sicimukondweletsa. (Yobu 4:18; 25:5)

Yehova amayamikila kudzipeleka kwathu (Yobu 36:5)

Munthu ndi wacabecabe kwa Mulungu (Yobu 22:2)

Yehova amavomeleza ndi kudalitsa utumiki wathu umene timacita mokhulupilika (Yobu 33:26; 36:11)

Mulungu alibe nazo nchito zakuti mukucita zinthu mwacilungamo (Yobu 22:3)

Yehova amayang’anila anthu olungama ndi okhulupilika (Yobu 36:7)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani