LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsa. 6
  • “Yamikani Yehova”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Yamikani Yehova”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Yamikani Yehova Ndipo Mudzadalitsidwa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Pemphelo la Mayamiko
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Muziyamika pa Ciliconse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Yang’anani kwa Yehova Kuti Akuthandizeni Kupilila na Kukutonthozani
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 August tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 106-109

“Yamikani Yehova”

Mose ndi Aisraeli ayamikila Yehova

N’cifukwa ciani Aisiraeli anaiŵala mwamsanga zimene Yehova anacita powapulumutsa?

106:7, 13, 14

  • Analeka kuika maganizo awo pa Yehova ndipo anayamba kuganizila kwambili zofuna zawo

N’ciani cingakuthandizeni kukhalabe ndi mtima woyamikila?

106:1-5

  • Muziganizila zinthu zosiyanasiyana zimene Mulungu wakucitilani

  • Muziganizila kwambili za ciyembekezo canu

  • Muzipeleka pemphelo loyamikila kwa Yehova, ndipo muzichula mwacindunji zimene wakucitilani

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani