LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsa. 6
  • Gogi wa Magogi Adzawonongedwa Posacedwa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Gogi wa Magogi Adzawonongedwa Posacedwa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 August tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EZEKIELI 35-38

Gogi wa Magogi Adzawonongedwa Posacedwa

Baibo imafotokoza zimene zidzacitika Gogi wa Magogi asanawonongedwe na pambuyo pake.

  • Kuwonongedwa kwa Babulo Wamkulu

    Chiv. 17:16-18

    Cisautso cacikulu cidzayamba na kuwonongedwa kwa

  • Asilikali a Gogi wa Magogi akonzekela kuukila anthu a Mulungu

    Ezek 38:2, 11, 15

    Anthu a Yehova adzaukilidwa na

  • Dzuŵa lawala pa dziko lapansi

    Chiv. 16:16

    Yehova adzawononga Gogi wa Magogi pa nkhondo ya

  • Christ on his heavenly throne

    Chiv. 20:4

    Khristu adzayamba ulamulilo wake wa

Ningakonzekele bwanji mwauzimu za kuukilidwa ndi Gogi wa Magogi?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani