LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsa. 7
  • Mmene Masomphenya a Ezekieli a Kacisi Amakukhudzilani

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mmene Masomphenya a Ezekieli a Kacisi Amakukhudzilani
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Kubwezeletsa Kulambila Koyela
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Ezekieli Anasangalala Polengeza Uthenga wa Mulungu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Mmene Yehova Amatithandizila Kugwila Nchito Yolalikila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Kuyenga Anthu a Mulungu Mwamakhalidwe—Kuonetsa Ciyelo ca Mulungu
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 August tsa. 7

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EZEKIELI 39-41

Mmene Masomphenya a Ezekieli a Kacisi Amakukhudzilani

40:10, 14, 16

  • Zipata zakunja za kum’mawa kwa kacisi zimene Ezekieli anaona m’masomphenya

    Zipinda za alonda na zipilala zazitali zitikumbutsa kuti miyezo ya Yehova ya kulambila koyela ni yapamwamba maningi

  • Anthu ayelekezela kuti aloŵa mu kacisi wa uzimu umene Ezekieli anaona

    Dzifunseni kuti, ‘Ningasunge bwanji miyezo ya Yehova yapamwamba ndi yolungama?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani